Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/12 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 19
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 19
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 3/12 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa March 19

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 19

Nyimbo Na. 58 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 3 ndime 12-18 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yeremiya 8-11 (Mph. 10)

Na. 1: Yeremiya 10:17-25 ndi Yeremiya 11:1-5 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kukumbukira Imfa ya Yesu?—rs tsa. 70 ndime 3 mpaka tsa. 71 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Zizindikiro za pa Chikumbutso Zimaimira Chiyani?—rs tsa. 71 ndime 3 mpaka tsa. 72 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 21

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 6:19-34. Kambiranani mmene mavesi amenewa angatithandizire mu utumiki.

Mph. 15: “Muzilalikira Molimba Mtima Kumalo a Ntchito ndi Amalonda.” Mafunso ndi mayankho. Funsani wofalitsa amene zinthu zimamuyendera bwino akamalalikira mu gawo la malonda.

Nyimbo Na. 108 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena