Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/12 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 26
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 26
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 3/12 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa March 26

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 26

Nyimbo Na. 96 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 4 ndime 1-4 ndi bokosi patsamba 30 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yeremiya 12-16 (Mph. 10)

Na. 1: Yeremiya 13:1-14 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Ndani Ali Oyenerera Kudya pa Mgonero wa Ambuye?—rs tsa. 72 ndime 3-4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mwambo Wokumbukira Imfa ya Yesu Uyenera Kuchitika Liti Ndiponso Kangati?—rs tsa. 73 ndime 2 mpaka tsa. 74 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 124

Mph. 5: Zilengezo. Dziwitsani mpingo magawo amene atsala kuti mugawireko timapepala toitanira anthu ku Chikumbutso.

Mph. 10: Musaiwale Kuchereza Alendo. (Aheb. 13:1, 2) Nkhani yokambidwa ndi mkulu. Kambiranani zimene mpingo wakonza zokhudza Chikumbutso. Fotokozani njira zothandiza zimene aliyense angatsatire kuti adzalandire bwino alendo ndiponso ofalitsa ofooka amene adzabwere pa Chikumbutso. Chitani chitsanzo chachidule cha mbali ziwiri. Poyamba, sonyezani wofalitsa akulandira munthu amene analandira kapepala koitanira anthu mwambowu usanayambe. Kenako mwambowu utatha, sonyezani wofalitsayo akukonza zoti adzakumanenso ndi mlendoyo kuti adzalimbikitse chidwi chake.

Mph. 20: “Kodi Yehova Amaona Chiyani mwa Ife?” Mafunso ndi mayankho. Kambiranani mmene mfundo za m’nkhaniyi zingatithandizire kuti tizichitirana zinthu moganizirana.

Nyimbo Na. 73 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena