Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/12 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 17
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 17
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 9/12 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa September 17

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 17

Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 12 ndime 9-13 ndi bokosi patsamba  97 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Ezekieli 46-48 (Mph. 10)

Na. 1: Ezekieli 48:1-14 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Nthawi Zonse Tifunika Kuchita Zinthu Moona Mtima?—Aef. 4:25, 28; 5:1 (Mph. 5)

Na. 3: Mmene Mungayankhire Ngati Wina Atanena Kuti, ‘A Mboni za Yehova Muli Ndi Baibulo Lanulanu’—rs tsa. 330 ndime 1-4 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 64

Mph. 30: “Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa—Kodi Ndidzachite Zotani Pamoyo Wanga? (Gawo 1)” Mafunso ndi mayankho. Gwiritsani ntchito mfundo zimene zili m’buku la Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri, tsamba 311 mpaka 317. Gwiritsani ntchito mawu opezeka m’ndime yoyamba ndi yomaliza monga mawu oyamba ndi omaliza pokambirana nkhaniyi.

Nyimbo Na. 88 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena