Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/13 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 28
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 28
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 1/13 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa January 28

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 28

Nyimbo Na. 11 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 18 ndime 6-11 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Mateyu 16-21 (Mph. 10)

Na. 1: Mateyu 17:22–18:10 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Ndi ‘Mawu Abwino’ ati a Yehova Amene Yoswa Anaona Akukwaniritsidwa?—Yos. 23:14 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Ndi Maulosi Ena ati Apadera a M’Baibulo Amene Sanakwaniritsidwebe?—rs tsa. 389 ndime 2–tsa. 390 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 134

Mph. 5: Yambitsani Phunziro la Baibulo Loweruka Loyambirira. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 4, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo, Loweruka loyambirira m’mwezi wa February. Limbikitsani ofalitsa onse kuti adzayesetse kuyambitsa maphunziro a Baibulo.

Mph. 25: “Kodi Tingatani Kuti Tipewe Imfa Zobwera Chifukwa cha Malungo?” Nkhani yokambirana ndi omvera yokambidwa ndi mkulu woyenerera. Pomaliza nkhaniyi bwerezani mfundo zimene mwakambirana pogwiritsa ntchito mafunso atatu amene ali kumapeto kwa nkhaniyi. Limbikitsani makolo kufunika kopita mwachangu kuchipatala ndi ana awo akayamba kuona zizindikiro za malungo.

Nyimbo Na. 53 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena