Ndandanda ya Mlungu wa March 25
MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 25
Nyimbo Na. 33 and Pemphero
□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:
bt mutu 20 ndime 16-20 (Mph. 30)
□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: Luka 4-6 (Mph. 10)
Na. 1: Luka 4:22-39 (Osapitirira mph. 4)
Na. 2: Kodi Mitundu ya Anthu Inachokera Kuti?—rs tsa. 234 ndime 2-tsa. 235 ndime 1 (Mph. 5)
Na. 3: Kodi Pali Umboni Wotani Wosonyeza Kuti Yesu Anaukitsidwa?—1 Akor. 15:3-7 (Mph. 5)
□ Msonkhano wa Utumiki:
Mph. 5: Yambitsani Phunziro la Baibulo Loweruka Loyambirira. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 8, chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka loyambirira m’mwezi wa April. Limbikitsani abale ndi alongo onse kuti adzayesetse kuyambitsa nawo maphunziro a Baibulo.
Mph. 25: “Gwiritsani Ntchito Kabuku Kakuti Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana ndime 6, chitani zitsanzo ziwiri.
Nyimbo Na. 97 ndi Pemphero