Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/13 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 25
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 25
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 3/13 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa March 25

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 25

Nyimbo Na. 33 and Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 20 ndime 16-20 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Luka 4-6 (Mph. 10)

Na. 1: Luka 4:22-39 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Mitundu ya Anthu Inachokera Kuti?—rs tsa. 234 ndime 2-tsa. 235 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Pali Umboni Wotani Wosonyeza Kuti Yesu Anaukitsidwa?—1 Akor. 15:3-7 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 111

Mph. 5: Yambitsani Phunziro la Baibulo Loweruka Loyambirira. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 8, chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka loyambirira m’mwezi wa April. Limbikitsani abale ndi alongo onse kuti adzayesetse kuyambitsa nawo maphunziro a Baibulo.

Mph. 25: “Gwiritsani Ntchito Kabuku Kakuti Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana ndime 6, chitani zitsanzo ziwiri.

Nyimbo Na. 97 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena