Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/15 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 30
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 30
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 3/15 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa March 30

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 30

Nyimbo Na. 58 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 10 ndime 18-21 ndi bokosi patsamba 106 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Samueli 14-15 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Samueli 14:36-45 (Osapitirira mph. 3)

Na. 2: Mapemphero Amene Mulungu Amayankha—bt tsa. 78-79 ndime 6-9 (Mph. 5)

Na. 3: Ulosi Wokhudza Masiku Otsiriza Ukukwaniritsidwa—igw tsa. 13 ndime 1 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: ‘Khalani Okonzekera Ntchito Iliyonse Yabwino.’​—Tito 3:1.

Nyimbo Na. 37

Mph. 15: Mavidiyo Enanso Opezeka pa Webusaiti Yathu Omwe Tingagwiritse Ntchito mu Utumiki. Nkhani yokambirana. Ikani vidiyo yakuti, Kodi Phunziro la Baibulo Limachitika Bwanji? Kambiranani kuti tingagwiritsire ntchito bwanji vidiyoyi mu utumiki. Kenako, chitaninso chimodzimodzi ndi vidiyo yakuti, Kodi pa Nyumba ya Ufumu Pamachitika Zotani? Pomaliza, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingachitire zimenezi. Ngati simungathe kuonetsa mavidiyowa, gwiritsani ntchito timapepala tomwe tinatuluka pamsonkhano wachigawo wa 2013 komanso 2014.

Mph. 15: “Muzigwiritsa Ntchito Kabuku Kakuti, Kodi M’Baibulo Muli Nkhani Zotani? Poyamba Kukambirana Ndi Anthu.” Mafunso ndi mayankho. Pemphani omvera kuti atchule njira zina zomwe tingagwiritsire ntchito kabukuka mu utumiki. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagwiritse ntchito kabukuka mu utumiki.

Nyimbo Na. 114 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena