Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 31
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 31
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa August 31

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 31

Nyimbo Na. 37 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 18 ndime 1-8 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 9-11 (8 min.)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (20 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: “Ine ndi a m’nyumba yanga, tizitumikira Yehova.”​—Yos. 24:15.

Nyimbo Na. 95

10 min: Zimene Munganene Pogawira Magazini a September. Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuchita zitsanzo zosonyeza zimene tinganene pogawira magaziniwa, pogwiritsa ntchito zitsanzo za ulaliki zomwe zili patsamba 4. Kenako kambiranani chitsanzo cha ulaliki chilichonse.

10 min: Kodi Mukulandira “Chakudya pa Nthawi Yoyenera?” Nkhani yochokera mu Nsanja ya Olonda ya August 15, 2014, tsamba 3 mpaka 5. Limbikitsani omvera kuti azigwiritsa ntchito zinthu zimene gulu latulutsa.

10 min: Kodi Muli Ndi Zolinga Zauzimu Zotani M’chaka cha Utumiki cha 2016? Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Gulu tsamba 118 ndime 3. Chitani chitsanzo chosonyeza banja likukambirana zolinga zauzimu zimene akufuna kukwaniritsa m’chaka cha utumiki cha 2016.

Nyimbo Na. 10 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena