Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsamba 4
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsamba 4

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda September 1

“Kodi mukudziwa komwe dzina lakuti, Mboni za Yehova linachokera? [Yembekezerani ayankhe.] Yankho la funsoli likupezeka m’Baibulo palemba limene limatiuza dzina la Mulungu. [Werengani Salimo 83:18.] A Mboni za Yehovafe timauza anthu uthenga wabwino wonena za Yehova komanso zimene adzachitire anthu m’tsogolo. Magazini iyi ili ndi mfundo zomwe zingakuthandizeni kudziwa zoona zokhudza a Mboni za Yehova.”

Galamukani! September

“Anthu ambiri amavomereza kuti anthufe timafunika ndalama kuti tithe kupeza zofunika pa moyo. Koma kodi mukuganiza kuti ndi bwino kukonda kwambiri ndalama? [Yembekezerani ayankhe.] Taonani zimene Baibulo limanena pa nkhaniyi. [Werengani 1 Timoteyo 6:9.] Magazini iyi ili ndi mfundo zomwe zingatithandize kuti tisamakonde kwambiri ndalama.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena