Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/15 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 2
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 2
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 10/15 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa November 2

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 2

Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 21 ndime 1-8 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 16-20 (8 min.)

Na. 1: 1 Mbiri 17:15-27 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kulalikira Mwakhama?​—bt tsa. 152 ndime 12-13 (5 min.)

Na. 3: Yehova Amadana ndi Anthu Achinyengo​—lv tsa. 168-169 ndime 15-17 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: Khalani “ozikika mozama” ndiponso ‘okhazikika m’chikhulupiriro.’​—Akol. 2:6, 7.

Nyimbo Na. 91

10 min: Zimene Munganene Pogawira Magazini a November. Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuchita zitsanzo ziwiri zosonyeza mmene tingagawirire magaziniwo pogwiritsa ntchito zitsanzo za ulaliki zimene zili patsamba lino. Kenako kambiranani zitsanzo za ulalikizo.

10 min: Zofunika pampingo.

10 min: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene anapindulira pogwiritsa ntchito malangizo a m’nkhani yakuti, “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muziphunzitsa Anthu Amene Mumaphunzira Nawo Baibulo Kuti Azikonda Kuphunzira Paokha.” Kenako apempheni kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zomwe anakumana nazo.

Nyimbo Na. 140 ndi Pemphero

Kumbukirani izi: Muyenera kuika nyimboyi kuti onse aimvetsere kenako muibwerezenso kuti onse aimbe nawo. Ngati simungakwanitse, imbani nyimbo nambala 44.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena