Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 4/09 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2009
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Kukachitika Ngozi Mumadziwitsa Ndani?
    Galamukani!—2009
  • Masamba a Kakombo Sanyowa
    Galamukani!—2009
  • Mzinda wa Bucharest Ndi Wochititsa Chidwi
    Galamukani!—2009
  • Ophunzira Ambiri Amapanikizika ndi Sukulu
    Galamukani!—2009
Onani Zambiri
Galamukani!—2009
g 4/09 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 2009

Mungatani Ngati Mumapanikizika ndi Sukulu Ndiponso Zinthu Zina?

N’chifukwa chiyani ana ambiri amapanikizika ndi sukulu? Kodi makolo ndi aphunzitsi angachite chiyani kuti awathandize?

3 Ophunzira Ambiri Amapanikizika ndi Sukulu

4 ‘Zochita Zandichulukira’

9 Kodi Makolo Mungathandize Bwanji Ana Anu?

11 Mzinda wa Bucharest Ndi Wochititsa Chidwi

16 Zimatheka Bwanji Kuphunzitsa Njovu?

19 Munthu Woyamba Kujambula Mapu a Dziko Lonse

23 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingatani Kuti Kuwerenga Baibulo Kuzindisangalatsa?

27 Panagona Luso!

Masamba a Kakombo Sanyowa

30 Zochitika Padzikoli

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Ana Amalikonda Bukuli

Kodi Kukachitika Ngozi Mumadziwitsa Ndani? 12

Kodi maphunziro a anthu othandiza anzawo pangozi amakhala otani? Kodi iwo amathandiza bwanji pakachitika ngozi? Werengani zimene munthu wina wogwira ntchito imeneyi ku Canada anafotokoza.

Kodi Kukhulupirika M’banja N’kutani? 28

Kodi kusirira mkazi kapena mwamuna wina n’koipa? Kodi mungapewe bwanji moyo wosakhulupirika m’banja?

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Taken by courtesy of City of Toronto EMS

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena