Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w08 3/1 tsamba 17
  • Kuwonongedwa kwa Sodomu ndi Gomora

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuwonongedwa kwa Sodomu ndi Gomora
  • Nsanja ya Olonda—2008
  • Nkhani Yofanana
  • Yesu Achiritsa Anthu Mozizwitsa
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Yesu Sanagonje Poyesedwa
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Yesu Anagometsa Anthu ndi Mawu Ake
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Petulo Akana Yesu
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—2008
w08 3/1 tsamba 17

Zoti Achinyamata Achite

Kuwonongedwa kwa Sodomu ndi Gomora

Malangizo: Chitani zotsatirazi muli pa malo opanda phokoso. Mukamawerenga mavesiwo, muziyerekezera kuti pamene zinthuzo zinkachitika inuyo munalipo. Yesani kuona nkhaniyi m’maganizo mwanu. Yerekezerani kuti mukumva mawu a m’nkhaniyi. Yesetsani kumva mu mtima mwanu ngati mmene ankamvera anthu a m’nkhaniyi.

ONANI BWINOBWINO NKHANIYI.​—WERENGANI GENESIS 19:1-14.

Ganizirani ndi kufotokoza maonekedwe a alendo a Loti.

․․․․․

Kodi ndi anthu otani amene anali pa gulu limene linafuna kupanga za chipongwe alendo a Loti?

․․․․․

FUFUZANI MOZAMA.​—WERENGANI GENESIS 13:7-13.

Kodi chinachitika n’chiyani kuti Loti azikhala ku Sodomu?

․․․․․

Kodi n’chifukwa chiyani Yehova anaona kuti n’koyenera kuwononga anthu okhala kumeneku?

․․․․․

WERENGANI GENESIS 19:15-26.

Kodi Yehova anasonyeza bwanji kum’komera mtima Loti?

․․․․․

Kodi n’chifukwa chiyani mkazi wa Loti anayang’ana m’mbuyo?

․․․․․

N’chifukwa chiyani anawonongedwa?

․․․․․

GWIRITSANI NTCHITO ZIMENE MWAPHUNZIRA. LEMBANI ZIMENE MWAPHUNZIRA PONENA ZA . . .

Mmene Yehova amaonera anthu ochita zoipa.

․․․․․

Chifundo cha Yehova.

․․․․․

Machenjezo amene Yehova amapereka asanalange anthu.

․․․․․

Kodi ndi mbali iti imene mwasangalala nayo kwambiri? Fotokozani chifukwa chake.

․․․․․

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena