Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w08 7/1 tsamba 31
  • Mkwiyo wa Kaini

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mkwiyo wa Kaini
  • Nsanja ya Olonda—2008
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwonongedwa kwa Sodomu ndi Gomora
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Yesu Achiritsa Anthu Mozizwitsa
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Yesu Anagometsa Anthu ndi Mawu Ake
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Yesu Sanagonje Poyesedwa
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—2008
w08 7/1 tsamba 31

Zoti Achinyamata Achite

Mkwiyo wa Kaini

Malangizo: Chitani zotsatirazi muli pa malo opanda phokoso. Mukamawerenga mavesiwo, muziyerekezera kuti pamene zinthuzo zinkachitika inuyo munalipo. Yesani kuona nkhanizi m’maganizo mwanu. Yerekezerani kuti mukumva mawu a m’nkhanizi. Yesani kuganizira mmene anthu otchulidwa m’nkhaniyi ankamvera.

ONANI BWINOBWINO NKHANI IYI.​—WERENGANI GENESIS 4:1-12.

Kodi mukuganiza kuti Kaini ankaoneka bwanji, ndipo anali ndi makhalidwe otani? Nanga bwanji Abele?

․․․․․

Kodi Kaini anaonetsa “ntchito za thupi” zotani, ndipo tikudziwa bwanji zimenezi? (Agalatiya 5:19-21)

․․․․․

FUFUZANI MOZAMA.​—WERENGANINSO MAVESI 4 MPAKA 7.

Kodi panalinso zinthu zina zimene Yehova anaganizira polandira kapena kukana nsembezi? (Miyambo 21:2)

․․․․․

Kodi mkwiyo ungakhale woyenera pazinthu zotani, koma n’chifukwa chiyani zinali zolakwika kuti Kaini ‘akwiye kwambiri’?

․․․․․

Kodi nsanje ingakhale yoyenera panthawi yotani, koma n’chifukwa chiyani nsanje ya Kaini inali yolakwika? (1 Mafumu 19:10)

․․․․․

Kodi Kaini akanachita chiyani kuti ‘alamulire’ mkwiyo wake?

․․․․․

GWIRITSANI NTCHITO ZIMENE MWAPHUNZIRA. LEMBANI ZIMENE MWAPHUNZIRA PONENA ZA . . .

Mkwiyo.

․․․․․

Nsanje.

․․․․․

Mmene mungalimbanirane ndi zizolowezi zoipa.

․․․․․

M’NKHANIYI, KODI NDI MFUNDO ZITI ZIMENE ZAKUKHUDZANI KWAMBIRI NDIPO N’CHIFUKWA CHIYANI?

․․․․․

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena