Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/94
  • Mbali ya Mafunso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mbali ya Mafunso
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
  • Nkhani Yofanana
  • Bokosi la Mafunso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2001
  • Mmene Phunziro la Buku la Mpingo Limatithandizira
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
  • Misonkhano Yokonzekera Utumiki Wakumunda
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Misonkhano Imene Imatilimbikitsa “pa Chikondi Ndi Ntchito Zabwino”
    Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
km 4/94

Mbali ya Mafunso

◼ Kodi Maphunziro Abuku Ampingo ayenera kuchititsidwa liti?

Kaŵirikaŵiri kumakhala kothandiza ndi koyenerera kukhala ndi magulu angapo a phunziro labuku okumana m’malo osiyanasiyana m’gawo lonse la mpingo mmalo moti aliyense adzisonkhana pa Nyumba Yaufumu. Maphunziro ameneŵa ayenera kuchititsidwa panthaŵi yoyenera koposa kwa unyinji wogaŵiridwa kufikapo. Kaŵirikaŵiri, limakhalapo madzulo a tsiku la mkati mwa mlungu pamene palibe misonkhano ina kapena ntchito yautumiki yolinganizidwa. Komabe, kungakhale kopindulitsa kukhala ndi phunziro labuku masana kuti padzifika okalamba amene amazengereza kuyenda kutada ndi ogwira ntchito usiku. M’zochitika zochepa, kungakhale kothandiza kukhala ndi phunziro lamasana kumapeto kwa mlungu.

Akulu angafufuze moyenerera kuti asankhe nthaŵi za misonkhano zimene zidzakhala ‘zokomera unyinji wa ofalitsa’ limodzinso ndi okondwerera. (om-CN tsa. 62) Nthaŵi yosankhidwayo iyenera kukhala pa tsiku ndi ola limene silidzasokoneza mosayenerera kapena kutsekereza makonzedwe olinganizidwa a utumiki wakumunda.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena