Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/03 tsamba 5
  • Pitaniko Mwamsanga

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitaniko Mwamsanga
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Nkhani Yofanana
  • M’pofunika Kumapitako Mwachangu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Kuchititsa Maphunziro a Baibulo Opita Patsogolo Gawo 11
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
  • Bokosi la Mafunso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Atumiki Olalikira Uthenga Wabwino
    Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
km 12/03 tsamba 5

Pitaniko Mwamsanga

Tipite mwamsanga kwa ndani? Kwa anthu amene amapempha mabuku kapena amene amatiuza kuti tiziwapititsira magazini nthaŵi zonse kapenanso amene akufuna kuti wa Mboni akawachezere kunyumba kwawo. Kodi amapempha zimenezi ndani? Anthu amene amalembera kalata ku ofesi ya nthambi kapena kuimbirako telefoni. Anthu akasonyeza chidwi chonchi, ofesi ya nthambi imadziŵitsa woyang’anira dera pomulembera kakalata kamene amakapatsa akulu a mpingo wapafupi kwambiri ndi kumene munthu wachidwiyo akukhala. Akulu akalandira kapepalaka, aziuza nthaŵi yomweyo wofalitsa amene akathandize munthu wachidwiyo dzina ndi kumene iye akukhala. Ngati wofalitsa akulephera kumupeza munthuyo panyumba, wofalitsayo angayese kupitakonso nthaŵi ina. Ngati mwapemphedwa kuyendera anthu achidwiŵa, yesetsani kuwapitira mwamsanga.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena