Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/14 tsamba 8
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Zitsanzo za Maulaliki a Utumiki wa Kumunda
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 12/14 tsamba 8

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda January 1

“Anthu ambiri amaona kuti nthawi zonse m’boma mumachitika zachinyengo. Koma kodi n’chiyani chimachititsa zimenezi? [Yembekezerani ayankhe.] Lemba ili likutithandiza kudziwa chifukwa chake. [Werengani Mlaliki 7:20.] Magaziniyi ikufotokoza zimene Baibulo limanena, zomwe zidzathandize kuti chinyengo chithe. Ngati mungakonde ndingakupatseni kuti mukaiwerenge.”

Galamukani! January

“Asayansi ena amakhulupirira kuti zinthu zamoyo zinachita kusintha kuchokera ku zinthu zina. Koma ena sakhulupirira zimenezi. Kodi inuyo mukuganiza kuti moyo unayamba bwanji? [Yembekezerani ayankhe.] Asayansi atafufuza kwa zaka zambiri, akuona kuti payenera kuti pali winawake amene analenga zamoyo. Zimenezitu zikugwirizana ndi zomwe Baibulo limanena. [Werengani Salimo 36:9.] Magaziniyi ikufotokoza chifukwa chake anthu ambiri amakhulupirira kuti zamoyo zinachita kulengedwa.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena