Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/15 tsamba 3
  • Tizinyamuka Tikangomaliza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizinyamuka Tikangomaliza
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Mungatani Kuti Msonkhano Wokonzekera Utumiki Uzikhala Wothandiza?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Bokosi la Mafunso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2001
  • Kodi Mukukwaniritsa Mbali Zonse za Utumiki Wanu?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Pindulani Mokwanira ndi Misonkhano Yokonzekera Utumiki wa Kumunda
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 1/15 tsamba 3

Tizinyamuka Tikangomaliza

Pa msonkhano wokonzekera utumiki wakumunda, timakumana ndi abale ndi alongo athu ndipo n’zosadabwitsa kuti timafuna kucheza nawo. Koma msonkhanowu ukangotha m’malo moyamba kucheza, tiyenera kunyamuka nthawi yomweyo n’kupita mu utumiki. Zili choncho chifukwa ntchito yathu ndi yofunika kuigwira mwamsanga. (2 Tim. 4:2) Ndi bwino kunyamuka nthawi yomweyo, kuti tisawononge nthawi yomwe tikanakhala tikulalikira. Timakhala ndi nthawi yambiri yokambirana zolimbikitsa ndi munthu amene tayenda naye, tikamachoka panyumba ina kupita panyumba ina. Tikamanyamuka msonkhano wokonzekera utumiki utangotha, zimasonyeza kuti timafunitsitsa kutumikira Yehova ndi Yesu mwakhama komanso monga akapolo.—Aroma 12:11.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena