Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 December tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • GALAMUKANI!
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • N’CHIFUKWA CHIYANI TIYENERA KUPHUNZIRA BAIBULO? (Vidiyo)
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 December tsamba 1
Alongo awiri akuchititsa phunziro la Baibulo ku Chile

Kuchititsa phunziro la Baibulo ku Chile

Zitsanzo za Ulaliki

GALAMUKANI!

Galamukani! Na. 6 2016 | Kodi Tingapewe Bwanji Matenda?

Funso: Anthu ambiri amafuna kukhala ndi moyo wathanzi. Kodi mukuganiza kuti tingatani kuti tidziteteze ku matenda?

Lemba: Miy. 22:3

Perekani Magaziniyo: Galamukani! iyi ikufotokoza njira zimene tingatsate kuti tidziteteze ku matenda.

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi Mulungu ndi amene amayambitsa mavuto amene timakumana nawo?

Lemba: Yobu 34:10

Zoona Zake: Mulungu si amene amachititsa mavuto athu. Amene amachititsa mavuto ndi Mdyerekezi komanso anthu amene amasankha zinthu molakwika. Ndipo nthawi zina timakumana ndi mavuto chifukwa choti tinali malo olakwika pa nthawinso yolakwika. Tikakumana ndi mavuto, Mulungu amakhala wokonzeka kutithandiza chifukwa amatidera nkhawa.

N’CHIFUKWA CHIYANI TIYENERA KUPHUNZIRA BAIBULO? (Vidiyo)

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo? (vidiyo)

Funso: Kodi mukuganiza kuti Mulungu ndi amene akulamulira dzikoli? [Yembekezerani kuti ayankhe.] Zimene Baibulo limanena zikhoza kukudabwitsani. Tiyeni tione zimenezi m’vidiyoyi. [Onetsani vidiyoyo.]

Perekani Buku: Mutu 11 wa buku ili ukufotokoza chifukwa chake Mulungu walola kuti anthu azivutika. Ukufotokozanso kuti Mulungu athetsa mavutowa posachedwapa. [Perekani buku lakuti, Zimene Baibulo Limaphunzitsa.]

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena