Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 October tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • GALAMUKANI!
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • KODI N’ZOONADI KUTI AKUFA ADZAUKA? (T-35)
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 October tsamba 1
M’bale akugawira kapepala kakuti Akufa Adzauka ku Tuvalu

Akugawira kapepala kakuti Akufa Adzauka? ku Tuvalu

Zitsanzo za Ulaliki

GALAMUKANI!

Galamukani! Na. 5 2017 | Zimene Tingachite Kuti Tipulumuke Pakachitika Ngozi Zadzidzidzi

Funso: N’chifukwa chiyani tiyenera kukonzekera ngozi zadzidzidzi?

Lemba: Miy. 27:12

Perekani Magaziniyo: Magazini iyi ikufotokoza zimene tingachite ngozi isanachitike, ikamachitika komanso pambuyo poti yachitika.

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi timasonyeza bwanji kuti timakonda Mulungu?

Lemba: 1 Yoh. 5:3

Zoona Zake: Timasonyeza kuti timakonda Mulungu tikamamvera malamulo ake.

KODI N’ZOONADI KUTI AKUFA ADZAUKA? (T-35)

Kodi N’zoonadi Kuti Akufa Adzauka?

Funso: Chaka chilichonse, anthu ambiri padziko lonse amachita miyambo yolemekeza akufa. Kodi n’zotheka kudzaonananso ndi achibale komanso anzathu amene anamwalira?

Lemba: Mac. 24:15

Perekani Kapepalako: Kapepala aka kakufotokoza mmene chiyembekezo choti akufa adzauka chingatithandizire. [Ngati n’kotheka, muonetseni vidiyo yakuti Kodi Anthu Amene Anamwalira Adzakhalanso ndi Moyo?]

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena