Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 September tsamba 3
  • Yesu Analalikira Mayi Wachisamariya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yesu Analalikira Mayi Wachisamariya
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Ndife Mboni za Yehova Nthawi Zonse
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Mukhoza Kukwanitsa Kulalikira Mwamwayi
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Lemekezani Yehova mwa Kulalikira Mwamwayi
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Mmene Tingayambire Ulaliki Wamwamwayi
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 September tsamba 3
Yesu akuyankhula ndi mayi wachisamariya pachitsime; mayi wachisamariya akuuza ena za Yesu

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 3-4

Yesu Analalikira Mayi Wachisamariya

4:6-26, 39-41

Kodi n’chiyani chinathandiza Yesu kuti alalikire mwamwayi?

  • 4:7​—Iye anayamba n’kupempha madzi m’malo moyamba ndi kumufotokozera za Ufumu wa Mulungu kapena kumudziwitsa kuti iyeyo ndi Mesiya

  • 4:9​—Yesu sanachite tsankho kwa mayi wachisamariya chifukwa cha mtundu wake

  • 4:9, 12​—Mayiyo atayambitsa nkhani zimene zikanachititsa kuti asemphane maganizo, Yesu anapewa nkhanizo mwanzeru n’kupitirizabe kukambirana naye nkhani yofunikirayo.​—cf 77 ¶3

  • 4:10​—Iye anayamba ndi chitsanzo cha zimene mayiyo ankachita tsiku ndi tsiku

  • 4:16-19​—Ngakhale kuti mayiyu anali wachiwerewere, Yesu ankamulemekezabe

Kodi nkhaniyi ikusonyeza bwanji kufunika kolalikira mwamwayi?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena