Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsamba 5
  • Kulalikira ndi Mashelefu Kwathandiza Anthu Ambiri Padziko Lonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulalikira ndi Mashelefu Kwathandiza Anthu Ambiri Padziko Lonse
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Zonsezi N’chifukwa Cha Kumwetulira Basi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Tingalalikire Bwanji Pogwiritsa Ntchito Tebulo Kapena Kashelefu Kamatayala?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Mulungu Wanditonthoza M’mayesero Anga Onse
    Galamukani!—2010
  • Lankhulani Ponena za Ulemerero wa Ufumu wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 November tsamba 5
Abale awiri akulalikira pogwiritsa ntchito kashelefu

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kulalikira ndi Mashelefu Kwathandiza Anthu Ambiri Padziko Lonse

Malinga ndi Machitidwe chaputala 5, Akhristu a m’nthawi ya atumwi ankapita kukachisi komwe kunkapezeka anthu ambiri n’cholinga choti akalalikire uthenga wabwino. (Mac. 5:19-21, 42) Masiku ano njira yolalikira m’malo opezeka anthu ambiri pogwiritsira ntchito kashelefu yathandiza anthu ambiri.

ONERANI VIDIYO YAKUTI KULALIKIRA NDI MASHELEFU KWATHANDIZA ANTHU AMBIRI PADZIKO LONSE, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Mi Jung You akulalikira pogwiritsa ntchito kashelefu; Jacob Salomé; Annies ndi mwamuna wake akulalikira pogwiritsa ntchito kashelefu

    Kodi njira yolalikira pogwiritsa ntchito kashelefu inayamba liti, nanga inayamba bwanji?

  • Kodi kulalikira pogwiritsa ntchito kashelefu kuli ndi ubwino wotani tikayerekezera ndi kugwiritsa ntchito tebulo?

  • Kodi tingaphunzire chiyani pa zimene zinachitikira Mi Jung You?

  • Kodi zimene zinachitikira Jacob Salomé zikusonyeza bwanji ubwino wolalikira pogwiritsa ntchito kashelefu?

  • Kodi zimene zinachitikira Annies ndi mwamuna wake zikutiphunzitsa chiyani pa nkhani ya mmene tingachitire tikamalalikira pogwiritsa ntchito kashelefu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena