Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsamba 7
  • Muzigwira Ntchito Yanu Mwaluso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzigwira Ntchito Yanu Mwaluso
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Sipanawonongeke Chilichonse
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Zinthu Zomwe Timagwiritsa Ntchito Pophunzitsa
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tiziphunzitsa Mfundo za Choonadi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Tizigwiritsa Ntchito Mwaluso Zinthu Zomwe Timagwiritsa Ntchito Pophunzitsa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 January tsamba 7
Munthu akugwiritsa ntchito chipangizo chopalira matabwa mwaluso.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

“Muzigwira Ntchito Yanu Mwaluso”

Kalipentala waluso amadziwa mmene angagwiritsire ntchito zipangizo zake. Mofanana ndi zimenezi, mtumiki wa Yehova amakhala “wantchito wopanda chifukwa chochitira manyazi ndi ntchito imene wagwira” ngati amadziwa kugwiritsira ntchito bwino Zinthu Zophunzitsira. (2 Tim. 2:15) Yankhani mafunso otsatirawa kuti muone ngati mumadziwa kugwiritsa ntchito bwino zinthu zomwe timagwiritsira ntchito pophunzira ndi anthu mu utumiki.

MVERANI MULUNGU KUTI MUDZAPEZE MOYO WOSATHA

  • Chikuto cha kabuku kakuti ‘Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha.’

    Kodi kabukuka tingakagwiritsire ntchito pophunzira ndi anthu ati?—mwb17.03 5 ¶1-2

  • Kodi tingakagwiritsire ntchito bwanji tikamaphunzira ndi anthu?​—km 7/12 3 ¶6

  • Kuwonjezera pa kabukuka, kodi ndi mabuku enanso ati omwe tiyenera kuphunzira ndi munthu kuti afike pobatizidwa?​—km 7/12 3 ¶7

UTHENGA WABWINO WOCHOKERA KWA MULUNGU

  • Chikuto cha kabuku kakuti ‘Uthenga Wabwino Wochokera Kwa Mulungu.’

    Kodi kabukuka ndi kosiyana bwanji ndi zinthu zina zomwe timagwiritsira ntchito pophunzira ndi anthu?​—km 3/13 4-5 ¶3-5

  • N’chiyani chomwe muyenera kuchita mukamagawira kabukuka?​—km 9/15 3 ¶1

  • Kodi mungagwiritsire ntchito bwanji kabukuka mukamaphunzira ndi anthu?​—mwb16.01 8

  • Kodi tingayambe liti kuphunzira buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa?—km 3/13 7 ¶10

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

  • Chikuto cha buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa.’

    Kodi tingagwiritsire ntchito bwanji mfundo zachidule za m’bukuli komanso mawu akumapeto?​—mwb16.11 5 ¶2-3

KODI NDANI AKUCHITA CHIFUNIRO CHA YEHOVA MASIKU ANO?

  • Chikuto cha kabuku kakuti ‘Kodi Ndani Akuchita Chifuniro Cha Yehova Masiku Ano?’

    Kodi tingayambe liti kuphunzira ndi munthu kabuku kameneka?​—mwb17.03 8 ¶1

  • Kodi kabukuka tingakagwiritsire ntchito bwanji?​—mwb17.03 8, kabokosi

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena