Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 July tsamba 14
  • Solomo Anapemphera Modzichepetsa Komanso Mochokera Pansi pa Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Solomo Anapemphera Modzichepetsa Komanso Mochokera Pansi pa Mtima
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Tizitamanda Yehova Chifukwa ndi Wanzeru
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Solomo Anali Mfumu Yanzeru
    Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?
  • Kodi Solomo Ndi Chitsanzo Chabwino Kapena Choipa?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Nzeru Ndi Zamtengo Wapatali
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 July tsamba 14
Solomo akupemphera patsogolo pa guwa lansembe pamaso pa anthu.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Solomo Anapemphera Modzichepetsa Komanso Mochokera Pansi pa Mtima

Pa mwambo wotsegulira kachisi Solomo anapereka pemphero lochokera pansi pa mtima pamaso pa anthu (1Mf 8:22; w09 11/15 9 ¶9-10)

Solomo anatamanda Yehova ndipo sanadzilemekeze yekha (1Mf 8:23, 24)

Solomo anapemphera modzichepetsa (1Mf 8:27; w99 1/15 17 ¶7-8)

Solomo anapereka chitsanzo chabwino kwambiri makamaka kwa anthu amene amapemphera m’malo mwa anthu ena pagulu. Tiziganizira kwambiri mmene Yehova akumvera pempherolo osati zimene anthu akumva.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena