Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 January tsamba 16
  • Khalani ndi Zolinga pa Nyengo ya Chikumbutso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani ndi Zolinga pa Nyengo ya Chikumbutso
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mwakonzeka Kudzapezekapo pa Tsiku Lofunika Kwambiri pa Chaka?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Yehova Amadalitsa Khama Lathu Loyesetsa Kuti Tipezeke pa Chikumbutso
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Zimene Mungachite Kuti Mudzasangalale M’nyengo ya Chikumbutso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Nyengo ya Chikumbutso Imatipatsa Mwayi Wowonjezera Utumiki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 January tsamba 16

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Khalani ndi Zolinga pa Nyengo ya Chikumbutso

Chaka chilichonse, anthu a Yehovafe timayembekezera kuchitira limodzi mwambo wa Chikumbutso. Chikumbutsocho chikatsala pang’ono kuchitika komanso pambuyo poti chachitika, timayesetsa kugwiritsa ntchito mwayi wapadera omwe timakhala nawo kuti titamande komanso kuthokoza Yehova chifukwa cha mphatso ya dipo. (Aef 1:3, 7) Mwachitsanzo timagwira nawo ndi mtima wonse ntchito yoitanira anthu ku mwambowu. Ena amakwanitsa kusintha zinthu zina pa moyo wawo n’cholinga choti achite upainiya wothandiza wa maola 30 kapena 50 m’mwezi wa March kapena April. Pa nyengo ya Chikumbutso ya chaka chino, kodi mungakonde mutawonjezera nthawi imene mumalalikira? N’chiyani chingakuthandizeni kuchita zimenezi?

Nthawi zambiri anthu timatha kuchita zambiri tikakonzekeratu. (Miy 21:5) Choncho popeza kuti nyengo ya Chikumbutso yayandikira, panopa ndi nthawi yabwino yoyamba kukonzekera. Ganizirani kuchuluka kwa nthawi yolalikira imene mungakonde kuwonjezera pa nyengo ya Chikumbutso kenako onani zimene mungachite kuti mukwanitse cholinga chanuchi. Mukatero pemphani Yehova kuti adalitse zimene mwasankhazo.​—1Yo 5:14, 15.

Kodi mungaganizire njira zina zimene zingakuthandizeni kuchita zambiri mu utumiki pa nyengo ya Chikumbutsoyi?

Zolinga

Zimene ndingachite kuti ndikwanitse zolinga zanga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena