Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 16
  • Kulimbikitsa Anthu Omwe Amatumikira pa Beteli

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulimbikitsa Anthu Omwe Amatumikira pa Beteli
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Zosankha Zomwe Zimasonyeza Kuti Timadalira Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Sitili Tokha
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
  • Muzikumbukira Yehova Yemwe ndi “Mulungu Wamoyo”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Tizivomereza Modzichepetsa Kuti Sitikudziwa Zonse
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 16

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kulimbikitsa Anthu Omwe Amatumikira pa Beteli

Aliyense amakumana ndi mavuto ndipo amafunika kutonthozedwa komanso kuthandizidwa. Ngakhale amene ndi olimba mwauzimu kapena amene ali ndi mwayi wapadera wautumiki, nawonso akhoza kufooka. (Yob 3:​1-3; Sl 34:19) Kodi tingaphunzire chiyani pa dongosolo lolimbikitsa anthu amene amatumikira pa Beteli?

ONERANI VIDIYO YAKUTI ‘TIZIDALIRA MULUNGU,’ KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi anthu a m’banja la Beteli amakumana ndi mavuto otani?

  • Kodi abale amachita zinthu 4 ziti kuti alimbikitse atumiki a pa Beteli?

  • Kodi abale amene amalimbikitsa atumiki a pa Beteli amapindula bwanji?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena