Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 9
  • Makolo, Muziphunzitsa Ana Anu Kudziwa Mmene Angasangalatsire Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Makolo, Muziphunzitsa Ana Anu Kudziwa Mmene Angasangalatsire Mulungu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Zosankha Zomwe Zimasonyeza Kuti Timadalira Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Muzigwiritsa Ntchito Mfundo za M’Baibulo Pothandiza Ana Anu Kuti Zinthu Ziwayendere Bwino
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Muziwerenga Baibulo Tsiku Lililonse Komanso Muzifunafuna Nzeru
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Zimene Tikuphunzira pa Mawu Omaliza a Amuna Okhulupirika
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 9
Zithunzi zosonyeza zinthu zophunzitsira ana: 1. Ana amisinkhu yosiyanasiyana akuona buku lakuti “Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo.” 2. Buku lakuti “Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo.” 3. Kamtsikana kanyamula buku lake lakuti “Buku Langa la Nkhani za M’Baibulo.” 4. Kamtsikana kena kakuwerenga buku la “Buku Langa la Nkhani za M’Baibulo.” 5. Mtsikana akuwerenga buku la Chingelezi lakuti “Your Youth​—⁠Getting the Best out of It” pa msonkhano. 6. Kamnyamata kakuchekenira chithunzi cha pa jw.org. 7. Chithunzi cha mu kabuku kakuti “Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo.” 8. Chithunzi cha Kalebe ndi Sofiya cha mu mavidiyo akuti “Khalani Bwenzi la Yehova.” 9. Buku lakuti “Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo.” Chithunzi cha m’bukuli chosonyeza Samisoni akukankha zipilala ziwiri ndi mphamvu zake zonse.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Makolo, Muziphunzitsa Ana Anu Kudziwa Mmene Angasangalatsire Mulungu

Yehova amaona kuti ana ndi amtengo wapatali. Iye amawaona akamakula mwauzimu komanso akamapirira. (1Sa 2:26; Lu 2:52) Ngakhale atakhala ang’ono, akhoza kumasangalatsa Yehova ngati ali ndi makhalidwe abwino. (Miy 27:11) Kudzera m’gulu lake, Yehova wapereka zinthu zabwino kwambiri zothandiza makolo kuphunzitsa ana awo kuti azimukonda komanso kumumvera.

ONERANI VIDIYO YAKUTI ANANU, YEHOVA AMASANGALALA MUKAMAPIRIRA, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi Yehova wakhala akuthandiza komanso kutsogolera bwanji achinyamata kwa zaka zambiri?

  • Kodi pali zinthu ziti zomwe zingathandize makolo?

  • Ngati ndinu wachinyamata, kodi Yehova wakupatsani zinthu ziti zomwe zakuthandizani, nanga n’chifukwa chiyani?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena