Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yb15 tsamba 176-192
  • Ziwerengero Zonse za 2014

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ziwerengero Zonse za 2014
  • Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
  • Nkhani Yofanana
  • Ziwerengero Zonse za 2015
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2016
  • Ziwerengero Zonse za 2013
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova 2014
  • Ziwerengero Zonse za 2016
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2017
  • Ziwerengero Zonse za 2012
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova 2013
Onani Zambiri
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
yb15 tsamba 176-192

Ziwerengero Zonse za 2014

  • Nthambi za Mboni za Yehova: 90

  • Mayiko Amene Anatumiza Lipoti: 239

  • Mipingo Yonse: 115,416

  • Opezeka pa Chikumbutso: 19,950,019

  • Amene Anadya Zizindikiro: 14,121

  • Chiwerengero Chapamwamba cha Ofalitsa Ufumu: 8,201,545

  • Avereji ya Ofalitsa Amene Analalikira Mwezi Uliwonse: 7,867,958

  • Peresenti ya Kuwonjezeka kwa Ofalitsa Kuchokera mu 2013: 2.2

  • Obatizidwa Onse: 275,581

  • Avereji ya Apainiya Othandiza Mwezi Uliwonse: 635,298

  • Avereji ya Apainiya Okhazikika Mwezi Uliwonse: 1,089,446

  • Maola Onse Amene Tinalalikira: 1,945,487,604

  • Avereji ya Maphunziro a Baibulo Mwezi Uliwonse: 9,499,933

M’chaka chautumiki cha 2014, a Mboni za Yehova anagwiritsa ntchito ndalama zoposa madola 224 miliyoni posamalira apainiya apadera, amishonale ndi oyang’anira oyendayenda. Padziko lonse pali abale ndi alongo okwana 24,711 amene akutumikira m’maofesi a nthambi. Onsewa ali m’gulu la Atumiki Apadera a Nthawi Zonse a Mboni za Yehova.

ZAKA ZIWIRI ZOYAMBIRIRA

Kuyambira pa August 27, 2012 kufika pa August 31, 2014

  • Chithunzi patsamba 177

    jw.org ikupezeka m’zilankhulo zoposa 540

  • Anthu akhoza kuchita dawunilodi zinthu m’zilankhulo zoposa 700

  • Chithunzi patsamba 177

    Anthu anapita nthawi zoposa 850,000,000 pa jw.org

  • Anthu anaona nkhani zoposa 4 biliyoni

  • Mafaelo oposa 1 biliyoni anachitidwa dawunilodi

  • Anthu anaonera kapena kuchita dawunilodi mavidiyo oposa 159 miliyoni

  • Anthu oposa 100,000 anapempha kuti aziphunzira Baibulo

    Chithunzi patsamba 177

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena