-
Afilipi 1:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Zidzatero mogwirizana n’kuti ndikudikira mwachidwi,+ ndiponso ndili ndi chiyembekezo+ chakuti sindidzachititsidwa manyazi+ mwa njira iliyonse. Koma kuti mwa ufulu wanga wonse wa kulankhula,+ Khristu alemekezedwe mwa thupi langa tsopano, monga mmene zakhala zikuchitikira m’mbuyo monsemu.+ Kaya ndikhala ndi moyo kapena ndimwalira.+
-