Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • kp tsamba 32
  • Mungathandizidwe Kumvetsetsa Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mungathandizidwe Kumvetsetsa Baibulo
  • Dikirani!
  • Nkhani Yofanana
  • “Pitiriza m’Zinthu Zimene Unaphunzira”
    Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi
  • ‘Ukhalebe mu Zimene Waziphunzira’
    “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Mungapeze buku lina
    Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
  • Mabuku Ogawira
    Kupulumuka Kuloŵa m’Dziko Lapansi Latsopano
Onani Zambiri
Dikirani!
kp tsamba 32

Mungathandizidwe Kumvetsetsa Baibulo

M’Baibulo muli zinthu zofunika kwambiri kwa inu.

• Limafotokoza zimene Mlengi amanena za cholinga cha moyo.

• Limapereka malangizo abwino kwambiri a zimene mungachite kuti muthe kulimbana ndi mavuto pa moyo wanu panopa.

• Limafotokoza zimene tiyenera kuchita kuti tidzakhale ovomerezeka kwa Mulungu akamadzaweruza anthu onse.

Maphunziro a Baibulo opitirira 5,000,000 akuchitika padziko lonse.

Nthaŵi ndi malo ochitira zimakhala zimene inuyo mungakonde. Phunzirolo N’LAULERE.

Tumizani pempho lanu ku adiresi ya kufupi ndi kwanu pa maadiresi amene ali m’munsiŵa, kapena funsani Mboni ya Yehova iliyonse m’dera lanu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena