Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • scl tsamba 31-33
  • Kuchotsa Osalapa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuchotsa Osalapa
  • Malemba Othandiza pa Moyo wa Chikhristu
Malemba Othandiza pa Moyo wa Chikhristu
scl tsamba 31-33

Kuchotsa Osalapa

N’chifukwa chiyani akulu ayenera kuteteza mpingo ku zinthu zoipa?

2Ti 2:16, 17; 2Pe 2:1, 2; Yuda 3, 4

Kodi khalidwe loipa la m’bale kapena mlongo lingakhudze bwanji mpingo wonse?

1Ak 5:1, 2, 5, 6

  • Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:

    • Yos 7:1, 4-14, 20-26​—Tchimo limene Kaini ndi banja lake anachita linachititsa kuti mtundu wonse ukumane ndi mavuto

    • Yon 1:1-16​—Mneneri Yona akanaphetsa anthu onse omwe anali naye muboti chifukwa cha kusamvera kwake

Kodi Mkhristu ayenera kupewa makhalidwe ati kuti asachotsedwe mumpingo?

Aro 16:17, 18; 1Ak 5:11; 1Ti 1:20; Tit 3:10, 11

Onaninso “Makhalidwe Amene Akhristu Ayenera Kukhala Nawo”

N’chiyani chiyenera kuchitika ngati Mkhristu wobatizidwa akupitirizabe kuchita tchimo lalikulu?

1Ak 5:11-13

Onaninso 1Yo 3:4, 6

Akamasamalira nkhani ya munthu yemwe wachita tchimo lalikulu, kodi akulu ayenera kukumbukira mfundo za mʼBaibulo ziti?

De 13:12-14; 17:2-4, 7; Mt 18:16; 2Ak 13:1; 1Ti 5:19

Onaninso Miy 18:13; 1Ti 5:21

N’chifukwa chiyani kuchotsa kapena kudzudzula anthu ena mumpingo n’koyenera? Nanga zimenezi zingathandize bwanji mpingo?

1Ak 5:3-6; 1Ti 5:20

Kodi Baibulo limanena kuti tizichita bwanji zinthu ndi anthu ochotsedwa?

Aro 16:17; 1Ak 5:11, 13

Kodi munthu yemwe anachotsedwa akalapa, zingatheke kuti abwerere mumpingo?

2Ak 2:6, 7

Onaninso “Kulapa”

Kodi tonsefe tingathandize bwanji kuti mpingo upitirize kukhala woyera?

Le 5:1; Ahe 12:15, 16

Onaninso De 13:6-11

N’chifukwa chiyani kungakhale kulakwitsa ngati Mkhristu atabisa tchimo lalikulu mwina chifukwa choopa kuchotsedwa?

Sl 32:1-5; Miy 28:13; Yak 5:14, 15

Onaninso “Tchimo​—Kuulula Machimo”

N’chifukwa chiyani nthawi zina ndi bwino kuchepetsa kucheza ndi munthu wochita zoipa ngakhale kuti sanachotsedwe?

1Ak 15:33; 2At 3:14

Kodi Mkhristu yemwe wanamiziridwa kapena mbiri yake yaipitsidwa angasankhe kuchita chiyani? Nanga n’chifukwa chiyani?

Mt 18:15-17, 21, 22; Akl 3:12-14; 1Pe 4:8

N’chifukwa chiyani Mkhristu wolimba mwauzimu ayenera kulangiza anthu amene akuchita zinthu mopanda nzeru?

Aga 6:1; Tit 2:3-5

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena