Genesis 36:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Anatenganso Basemati,+ yemwe anali mwana wamkazi wa Isimaeli, komanso anali mlongo wake wa Nebayoti.+ Yesaya 60:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Nkhosa zonse za ku Kedara+ zidzasonkhanitsidwa kwa iwe. Nkhosa zamphongo za ku Nebayoti+ zidzakutumikira.+ Ine ndidzazilandira paguwa langa lansembe,+ ndipo ndidzakongoletsa nyumba yanga yokongola.+
3 Anatenganso Basemati,+ yemwe anali mwana wamkazi wa Isimaeli, komanso anali mlongo wake wa Nebayoti.+
7 Nkhosa zonse za ku Kedara+ zidzasonkhanitsidwa kwa iwe. Nkhosa zamphongo za ku Nebayoti+ zidzakutumikira.+ Ine ndidzazilandira paguwa langa lansembe,+ ndipo ndidzakongoletsa nyumba yanga yokongola.+