Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 34:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma pa tsiku lachitatu, pamene anthuwo anali pa ululu,+ ana awiri a Yakobo, Simiyoni ndi Levi,+ alongo ake a Dina,+ aliyense anatenga lupanga lake n’kukalowa mumzindawo mosaonetsera cholinga chawo. Kenako anayamba kupha mwamuna aliyense.+

  • Genesis 49:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Simiyoni ndi Levi m’pachibale pawo.+ Malupanga awo ndiwo zida zochitira zachiwawa.+

  • Ekisodo 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Awa ndi mayina a ana aamuna a Levi,+ malinga ndi mzere wobadwira wa makolo awo:+ Gerisoni, Kohati ndi Merari.+ Ndipo Levi anakhala ndi moyo zaka 137.

  • Numeri 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Ine ndikutenga Alevi pakati pa ana a Isiraeli m’malo mwa ana onse oyamba kubadwa+ a ana a Isiraeli ndipo iwo akhala anga.

  • 1 Mbiri 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ana a Levi+ anali Gerisoni,+ Kohati,+ ndi Merari.+

  • Chivumbulutso 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mu fuko la Simiyoni,+ 12,000.

      Mu fuko la Levi,+ 12,000.

      Mu fuko la Isakara,+ 12,000.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena