Genesis 49:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pagulu lawo, moyo wanga usakhale nawo.+ Maganizo anga asagwirizane ndi mpingo wawo,+ chifukwa atakwiya anapha anthu,+ ndipo mwankhanza zawo, anapundula* ng’ombe zamphongo. Genesis 49:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Utembereredwe mkwiyo wawo+ chifukwa ndi wankhanza,+ ndi ukali wawo chifukwa umachita mwachiwawa.+ Ndidzawamwaza mwa Yakobo, ndipo ndidzawabalalitsa mwa Isiraeli.+ Salimo 140:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Anthu amene amakonza chiwembu mumtima mwawo,+Amene amandiukira tsiku lonse ngati mmene zimakhalira pankhondo.+ Mika 2:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 “Tsoka kwa anthu amene amati akagona pabedi, amakonza chiwembu ndiponso kuganiza mmene angachitire zoipa.+ M’mawa kukangocha, iwo amazichitadi+ chifukwa chakuti ali ndi mphamvu zochitira zimenezo.+
6 Pagulu lawo, moyo wanga usakhale nawo.+ Maganizo anga asagwirizane ndi mpingo wawo,+ chifukwa atakwiya anapha anthu,+ ndipo mwankhanza zawo, anapundula* ng’ombe zamphongo.
7 Utembereredwe mkwiyo wawo+ chifukwa ndi wankhanza,+ ndi ukali wawo chifukwa umachita mwachiwawa.+ Ndidzawamwaza mwa Yakobo, ndipo ndidzawabalalitsa mwa Isiraeli.+
2 Anthu amene amakonza chiwembu mumtima mwawo,+Amene amandiukira tsiku lonse ngati mmene zimakhalira pankhondo.+
2 “Tsoka kwa anthu amene amati akagona pabedi, amakonza chiwembu ndiponso kuganiza mmene angachitire zoipa.+ M’mawa kukangocha, iwo amazichitadi+ chifukwa chakuti ali ndi mphamvu zochitira zimenezo.+