Genesis 28:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Ine ndili nawe ndipo ndikuyang’anira pa ulendo wako wonse, kufikira ndidzakubwezera kumalo ano.+ Sindidzakusiya kufikira nditachitadi zimene ndanena kwa iwe.”+ Genesis 31:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Kenako, mngelo wa Mulungu woona anandiitana m’malotowo kuti, ‘Yakobo!’ Ine ndinayankha kuti, ‘Ine pano.’+ Ekisodo 15:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Mwa kukoma mtima kwanu kosatha, mwatsogolera anthu amene munawawombola.+Mwa mphamvu yanu, inu mudzatengera anthu anu kudziko lanu lopatulika kumene mudzakhala.+ Yobu 19:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ineyo ndikudziwa bwino kuti wondiwombola+ ali moyo,Ndipo adzabwera pambuyo panga n’kuimirira+ pafumbi. Salimo 34:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Mngelo wa Yehova amamanga msasa mozungulira onse oopa Mulungu,+Ndipo amawapulumutsa.+
15 Ine ndili nawe ndipo ndikuyang’anira pa ulendo wako wonse, kufikira ndidzakubwezera kumalo ano.+ Sindidzakusiya kufikira nditachitadi zimene ndanena kwa iwe.”+
11 Kenako, mngelo wa Mulungu woona anandiitana m’malotowo kuti, ‘Yakobo!’ Ine ndinayankha kuti, ‘Ine pano.’+
13 Mwa kukoma mtima kwanu kosatha, mwatsogolera anthu amene munawawombola.+Mwa mphamvu yanu, inu mudzatengera anthu anu kudziko lanu lopatulika kumene mudzakhala.+
25 Ineyo ndikudziwa bwino kuti wondiwombola+ ali moyo,Ndipo adzabwera pambuyo panga n’kuimirira+ pafumbi.