Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho, a m’chigawo cha mafuko atatu cha ana a Yuda ndiwo anayamba kunyamuka m’magulu awo.+ Mtsogoleri wa asilikali awo anali Naasoni,+ mwana wa Aminadabu.

  • Deuteronomo 33:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Popitiriza, iye anapereka dalitso lotsatirali kwa Yuda,+ kuti:

      “Inu Yehova, imvani mawu a Yuda,+

      M’bweretseni kwa anthu ake.

      Manja ake amenya nkhondo pofuna kulanditsa zinthu zake.

      Mukhaletu mthandizi wake kwa adani ake.”+

  • 2 Samueli 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho akulu onse+ a Isiraeli anabwera kwa mfumu ku Heburoni, ndipo Mfumu Davide anachita nawo pangano+ ku Heburoni pamaso pa Yehova. Kenako iwo anadzoza+ Davide kukhala mfumu ya Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena