Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti ine ndinali mwana wabwino kwa bambo anga.+ Ndinali wokondedwa kwambiri ndiponso mmodzi yekhayo pamaso pa mayi anga.+

  • Miyambo 8:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 ine ndinali pambali pake monga mmisiri waluso.+ Tsiku ndi tsiku, iye anali kusangalala kwambiri ndi ine.+ Ineyo ndinkakhala wosangalala pamaso pake nthawi zonse.+

  • Yohane 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Pakuti Mulungu anakonda+ kwambiri dziko mwakuti anapereka Mwana wake wobadwa yekha,+ kuti aliyense wokhulupirira+ iye asawonongeke,+ koma akhale ndi moyo wosatha.+

  • Yohane 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chimene Atate amandikondera n’chakuti,+ ndikupereka moyo wanga+ kuti ndikaulandirenso.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena