Salimo 106:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Iwo anayamba kulambira Baala wa ku Peori,+Ndi kudya nsembe zoperekedwa ku zinthu zakufa.+ Ezekieli 18:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 ngati sadya+ zinthu zoperekedwa nsembe kwa mafano m’mapiri,+ ngati sakweza maso ake kuyang’ana mafano onyansa a nyumba ya Isiraeli,+ ngati saipitsa mkazi wa mnzake,+ ngati sayandikira mkazi amene wadetsedwa,+ 2 Akorinto 6:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Musamangidwe m’goli ndi osakhulupirira, chifukwa ndinu osiyana.+ Pali ubale wotani pakati pa chilungamo ndi kusamvera malamulo?+ Kapena pali kugwirizana kotani pakati pa kuwala ndi mdima?+ Chivumbulutso 2:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 “‘Komabe, ndakupeza ndi mlandu uwu. Walekerera mayi uja Yezebeli,+ amene amadzitcha mneneri. Iye amaphunzitsa+ ndi kusocheretsa akapolo anga+ kuti azichita dama+ ndi kudya zinthu zoperekedwa nsembe kwa mafano.+
6 ngati sadya+ zinthu zoperekedwa nsembe kwa mafano m’mapiri,+ ngati sakweza maso ake kuyang’ana mafano onyansa a nyumba ya Isiraeli,+ ngati saipitsa mkazi wa mnzake,+ ngati sayandikira mkazi amene wadetsedwa,+
14 Musamangidwe m’goli ndi osakhulupirira, chifukwa ndinu osiyana.+ Pali ubale wotani pakati pa chilungamo ndi kusamvera malamulo?+ Kapena pali kugwirizana kotani pakati pa kuwala ndi mdima?+
20 “‘Komabe, ndakupeza ndi mlandu uwu. Walekerera mayi uja Yezebeli,+ amene amadzitcha mneneri. Iye amaphunzitsa+ ndi kusocheretsa akapolo anga+ kuti azichita dama+ ndi kudya zinthu zoperekedwa nsembe kwa mafano.+