Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 25:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 M’Likasamo uikemo umboni umene ndidzakupatsa.+

  • Ekisodo 31:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno atamaliza kulankhula naye paphiri la Sinai, anapatsa Mose miyala iwiri yosema ya Umboni,+ miyala yolembedwapo mawu ndi chala cha Mulungu.+

  • Ekisodo 34:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndiyeno Mose anatsika m’phiri la Sinai atanyamula miyala iwiri ija ya Umboni m’manja mwake,+ koma iye sanadziwe kuti nkhope yake inali kuwala chifukwa anali atalankhula ndi Mulungu.+

  • Numeri 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno Mose anakaika ndodozo pamaso pa Yehova m’chihema cha Umboni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena