9 “Ndiyeno upange bwalo+ la chihema chopatulika. Kumbali ya ku Negebu, chakum’mwera, bwalolo ulitchinge ndi mpanda wa nsalu za ulusi wopota wabwino kwambiri.+ Mpandawo ukhale mikono 100 m’litali mwake kumbali imodziyo.
9 Ndiyeno anapanga bwalo la chihema chopatulika.+ Kumbali ya ku Negebu, chakum’mwera, bwalolo analitchinga ndi mpanda wa nsalu za ulusi wopota wabwino kwambiri. Mpandawo unali mikono 100 kutalika kwake kumbali imodziyo.+