Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 11:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 ndipo mwana aliyense woyamba kubadwa+ m’dziko la Iguputo adzafa. Kuyambira mwana woyamba wa Farao, amene wakhala pampando wachifumu, mpaka mwana woyamba wa kapolo wamkazi wokhala pamphero ndiponso mwana woyamba kubadwa wa nyama iliyonse.+

  • Numeri 3:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti mwana aliyense woyamba kubadwa ndi wanga.+ M’tsiku limene ndinapha mwana aliyense woyamba kubadwa m’dziko la Iguputo,+ ndinadzipatulira mwana aliyense woyamba kubadwa pakati pa Aisiraeli, kuyambira munthu mpaka chiweto.+ Amenewa azikhala anga. Ine ndine Yehova.”

  • Salimo 135:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Wochita zimenezi ndiye anapha ana oyamba kubadwa a ku Iguputo,+

      Anapha ana a anthu ngakhalenso ana a nyama.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena