-
Ekisodo 13:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Koma Farao anaumitsa mtima wake posalola kuti ife tichoke,+ motero Yehova anapha mwana woyamba kubadwa aliyense m’dziko la Iguputo,+ kuyambira mwana woyamba kubadwa wa munthu mpaka mwana woyamba kubadwa wa nyama.+ N’chifukwa chake tikupereka nsembe kwa Yehova ana onse a nyama oyamba kubadwa,+ ndipo tikuwombola mwana woyamba kubadwa aliyense mwa ana athu.’+
-
-
Salimo 136:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Yamikani amene anakantha Aiguputo mwa kupha ana awo oyamba kubadwa:+
Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+
-