Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 16:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndipo ana a Isiraeli anali kunena kwa Mose ndi Aroni kuti: “Zikanakhala bwino dzanja la Yehova likanatiphera+ m’dziko la Iguputo, kumene tinali kudya nyama+ ndipo tinali kudya mkate ndi kukhuta. M’malomwake mwatibweretsa m’chipululu muno kuti muphetse mpingo wonsewu ndi njala.”+

  • Ekisodo 17:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho anthu anamva ludzu pamenepo, ndipo anthuwo anapitiriza kung’ung’udzira Mose kuti: “N’chifukwa chiyani unatitulutsa mu Iguputo kuti udzatiphe ndi ludzu, ifeyo pamodzi ndi ana athu ndi ziweto zathu?”+

  • Numeri 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ana onse a Isiraeli anayamba kudandaula za Mose ndi Aroni.+ Ndipo khamu lonselo linati: “Zikanakhala bwino tikanangofera ku Iguputo, kapena tikanangofera m’chipululu muno.

  • Salimo 106:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Makolo athu ku Iguputo,

      Sanasonyeze kuzindikira kulikonse ntchito zanu zodabwitsa.+

      Sanakumbukire kuchuluka kwa kukoma mtima kwanu kosatha,+

      Koma anapanduka panyanja, pafupi ndi Nyanja Yofiira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena