Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndipo ngalande za pansi pa nyanja zinaonekera,+

      Maziko a dziko lapansi+ anakhala poonekera,

      Zinatero chifukwa cha kudzudzula kwa Yehova, chifukwa cha mphamvu ya mpweya wa m’mphuno mwake.+

  • Salimo 18:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndipo ngalande za pansi pa madzi zinaonekera,+

      Maziko a dziko lapansi anakhala poonekera.+

      Zinatero chifukwa cha kudzudzula kwanu, inu Yehova, chifukwa cha mphamvu ya mpweya wa m’mphuno mwanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena