Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye amadzutsa wonyozeka, kumuchotsa pafumbi.+

      Amachotsa osauka padzala,+

      Kuti awakhazike pakati pa anthu olemekezeka,+ ndipo amawapatsa mpando wachifumu waulemerero.+

      Pakuti michirikizo ya dziko lapansi ndi ya Yehova,+

      Ndipo anakhazika dziko lapansi pamichirikizo imeneyo.

  • 1 Mbiri 16:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Njenjemerani ndi mantha* pamaso pake, inu anthu nonse okhala padziko lapansi!

      Ndiponso dziko lapansi ndi lokhazikika,

      Silidzagwedezeka ku nthawi zonse.+

  • Salimo 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye adzaweruza anthu padziko lapansi mwachilungamo.+

      Adzazenga mlandu mitundu ya anthu moyenerera.+

  • Salimo 33:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Onse okhala padziko lapansi aope Yehova.+

      Anthu onse okhala panthaka ya dziko lapansi achite naye mantha.+

  • Salimo 77:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Phokoso la bingu lanu linali ngati la mawilo a galeta.+

      Mphezi zinaunika padziko.+

      Ndipo dziko lapansi linagwedezeka ndi kuyamba kunjenjemera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena