Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “‘Usamayendeyende pakati pa anthu amtundu wako n’kumachita miseche.+ Usachite kanthu kalikonse kuti uphetse mnzako.+ Ine ndine Yehova.

  • Deuteronomo 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “‘Usapereke umboni wonamizira mnzako.+

  • Deuteronomo 19:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Munthu akakonzera mnzake chiwembu mwa kupereka umboni wonama wakuti waphwanya lamulo,+

  • Salimo 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye sanena miseche ndi lilime lake.+

      Sachitira mnzake choipa,+

      Ndipo satonza bwenzi lake lapamtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena