Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 35:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mukasankhe mizinda yoyenerera kwa inu, kuti ikakhale mizinda yanu yothawirako. Munthu amene wapha mnzake mwangozi azikathawira kumeneko.+

  • Deuteronomo 4:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 kuti munthu wopha mnzake mwangozi,+ amene sanali kudana naye kale n’kale,+ azithawirako. Ameneyu azithawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi ndi kukhala ndi moyo.+

  • Deuteronomo 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Udzadzilambulire njira yopita kumizindayo ndipo udzagawe dziko limene Yehova Mulungu wako wakupatsa kuti likhale lako. Dzikolo udzaligawe m’zigawo zitatu. Wopha munthu azithawira kumizinda imeneyo.+

  • Yoswa 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho anasankha mizinda ina kuti ikhale yopatulika. Mizinda yake inali Kedesi+ ku Galileya m’dera lamapiri la Nafitali, Sekemu+ m’dera lamapiri la Efuraimu, Kiriyati-ariba,+ kutanthauza Heburoni, m’dera lamapiri la Yuda.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena