Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho muwoloke Yorodano+ ndi kukhala m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kukhala lanu.+ Iye adzakupumitsani kwa adani anu onse okuzungulirani, ndipo mudzakhaladi otetezeka.+

  • Salimo 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndidzagona pansi ndi kupeza tulo mu mtendere,+

      Pakuti inu nokha Yehova mumandichititsa kukhala wotetezeka.+

  • Miyambo 1:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Koma munthu wondimvera adzakhala mwabata+ ndipo sadzasokonezeka chifukwa choopa tsoka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena