Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 25:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chaka cha 50 chizikhala chopatulika, ndipo muzilengeza ufulu* kwa anthu onse okhala m’dzikolo.+ Chizikhala Chaka cha Ufulu+ kwa inu, ndipo aliyense wa inu azibwerera kumalo ake ndi kubanja lake.+

  • Levitiko 25:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Iye aziwerengera wom’gulayo zaka zotsala kuchokera pamene anadzigulitsa kukafika Chaka cha Ufulu,+ ndipo ndalama zimene anam’gulira zizigwirizana ndi kuchuluka kwa zaka.+ Azim’gwirira ntchito mofanana ndi waganyu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena