Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 6:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 “Uza Aroni ndi ana ake kuti, ‘Lamulo la nsembe yamachimo+ lili motere: Nyama ya nsembe yamachimo iziphedwa pamaso pa Yehova, pamalo+ ophera nyama ya nsembe yopsereza nthawi zonse. Chimenechi ndi chinthu chopatulika koposa.+

  • Levitiko 14:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndipo azipha nkhosa yaing’ono yamphongoyo pamalo+ amene nthawi zonse amapherapo nyama ya nsembe yamachimo ndi nsembe yopsereza, pamalo oyera.+ Azichita zimenezi chifukwa nsembe ya kupalamula ndi ya wansembe+ mofanana ndi nsembe yamachimo. Nsembe ya kupalamula ndi yopatulika koposa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena