Salimo 51:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Mundisambitse bwinobwino ndi kuchotsa cholakwa changa,+Ndiyeretseni ku tchimo langa.+ Yeremiya 33:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ndiwayeretsa ku zolakwa zawo zonse zimene anachimwa nazo pamaso panga,+ ndipo ndiwakhululukira zolakwa zawo zonse zimene anandichimwira nazo ndi kuphwanya nazo malamulo anga.+ Ezekieli 36:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ine ndidzakuwazani madzi oyera ndipo mudzakhala oyera. Ndidzakuyeretsani+ pokuchotserani zonyansa zanu zonse+ ndi mafano anu onse onyansa.+ Aefeso 5:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 ndipo anauyeretsa+ pousambitsa m’madzi a mawu a Mulungu.+ Aheberi 9:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 kuli bwanji magazi+ a Khristu, amene anadzipereka wopanda chilema kwa Mulungu kudzera mwa mzimu wamuyaya?+ Kodi magazi amenewo sadzayeretsa+ zikumbumtima zathu ku ntchito zakufa,+ kuti tichite utumiki wopatulika+ kwa Mulungu wamoyo? Aheberi 10:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Zikanakhala choncho, kodi nsembezo sakanasiya kuzipereka? Akanasiya chifukwa chakuti anthu ochita utumiki wopatulika, amene akanayeretsedwa kwathunthu kamodzi n’kamodziwo, sakanakhalanso ndi chikumbumtima chakuti ndi ochimwa.+
8 Ndiwayeretsa ku zolakwa zawo zonse zimene anachimwa nazo pamaso panga,+ ndipo ndiwakhululukira zolakwa zawo zonse zimene anandichimwira nazo ndi kuphwanya nazo malamulo anga.+
25 Ine ndidzakuwazani madzi oyera ndipo mudzakhala oyera. Ndidzakuyeretsani+ pokuchotserani zonyansa zanu zonse+ ndi mafano anu onse onyansa.+
14 kuli bwanji magazi+ a Khristu, amene anadzipereka wopanda chilema kwa Mulungu kudzera mwa mzimu wamuyaya?+ Kodi magazi amenewo sadzayeretsa+ zikumbumtima zathu ku ntchito zakufa,+ kuti tichite utumiki wopatulika+ kwa Mulungu wamoyo?
2 Zikanakhala choncho, kodi nsembezo sakanasiya kuzipereka? Akanasiya chifukwa chakuti anthu ochita utumiki wopatulika, amene akanayeretsedwa kwathunthu kamodzi n’kamodziwo, sakanakhalanso ndi chikumbumtima chakuti ndi ochimwa.+