Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 38:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno Yuda ataziyang’anitsitsa, ananena kuti:+ “Mkaziyu ndi wolungama koposa ine,+ chifukwa sindinam’pereke kwa mwana wanga Shela.”+ Zitatero, Yuda sanagone nayenso.+

  • Levitiko 20:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mwamuna akagona ndi mpongozi wake wamkazi, onse awiri aziphedwa ndithu.+ Iwo achita chinthu chosemphana ndi chibadwa. Mlandu wa magazi awo ukhale wa iwo eni.+

  • Ezekieli 22:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Munthu wachita zinthu zonyansa ndi mkazi wa mnzake,+ ndipo munthu wachita khalidwe lotayirira mwa kugona ndi mkazi wa mwana wake.+ Munthu wagona ndi mlongo wake, mwana wamkazi wa bambo ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena